ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا * - فهرس التراجم


ترجمة معاني آية: (24) سورة: الكهف
إِلَّآ أَن يَشَآءَ ٱللَّهُۚ وَٱذۡكُر رَّبَّكَ إِذَا نَسِيتَ وَقُلۡ عَسَىٰٓ أَن يَهۡدِيَنِ رَبِّي لِأَقۡرَبَ مِنۡ هَٰذَا رَشَدٗا
“Koma (utsogoze liwu lakuti): Insha Allah, (Allah akafuna!)” Ndipo mukumbuke Mbuye wako ukaiwala ponena kuti: “Mwina Mbuye wanga anditsogolera pa njira yapafupi pachiongoko kuposa iyi.”[258]
[258] Ayuda adamufunsa Mneneri (s.a.w) zankhani ya anyamata a kuphangawo. Iye adayankha kuti: “Ndikuuzani mawa,” sadanene kuti Allah akafuna ndikuuzani mawa.”
Choncho chivumbulutso sichidadze kwa iye ndipo anavutika kwambiri kusowa chowauza anthu aja. Kenako Allah adamuuza zoti ngati unena pa chinthu kuti chimenechi ndichichita mawa, nenanso mawu oti ngati Allah afuna.
التفاسير العربية:
 
ترجمة معاني آية: (24) سورة: الكهف
فهرس السور رقم الصفحة
 
ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا - فهرس التراجم

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

إغلاق