ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا * - فهرس التراجم


ترجمة معاني آية: (8) سورة: النساء
وَإِذَا حَضَرَ ٱلۡقِسۡمَةَ أُوْلُواْ ٱلۡقُرۡبَىٰ وَٱلۡيَتَٰمَىٰ وَٱلۡمَسَٰكِينُ فَٱرۡزُقُوهُم مِّنۡهُ وَقُولُواْ لَهُمۡ قَوۡلٗا مَّعۡرُوفٗا
Ndipo panthawi yogawa, ngati angabwere achibale, amasiye ndi osauka (omwe alibe gawo pa chumacho), apatseniko kanthu ndi kunena nawo mawu abwino.[111]
[111] Chuma nchinthu chimene chimachotsa moyo wa munthu mmalomwake, makamaka ngati chikupezeka m’njira yaulere yosachivutikira, monga chilili chuma chamasiye. Choncho amene alibepo gawo pa chumacho amangoti diso tong’o, kusilira. Ndipo nchifukwa chake Allah apa akunena kuti pogawa chuma chamasiyecho ngati achibale atabwerapo omwe alibepo gawo pa chumacho, awapatseko kachinthu kochepa ndi kuwapepesa kuti chomwe awapatsacho nchochepa.
التفاسير العربية:
 
ترجمة معاني آية: (8) سورة: النساء
فهرس السور رقم الصفحة
 
ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا - فهرس التراجم

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

إغلاق