Qurani Kərimin mənaca tərcüməsi - Şişyo dilinə tərcümə * - Tərcumənin mündəricatı


Mənaların tərcüməsi Ayə: (109) Surə: ən-Nisa
هَٰٓأَنتُمۡ هَٰٓؤُلَآءِ جَٰدَلۡتُمۡ عَنۡهُمۡ فِي ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَا فَمَن يُجَٰدِلُ ٱللَّهَ عَنۡهُمۡ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِ أَم مَّن يَكُونُ عَلَيۡهِمۡ وَكِيلٗا
Taonani! Inu ndi amene mwaayikira kumbuyo pa moyo wa pa dziko lapansi. Kodi ndani amene adzatsutsana ndi Allah pa iwo tsiku lachimaliziro, kapena ndani adzakhale mtetezi wawo.[143]
[143] M’ndime iyi Allah akuletsa anthu kuti asakhalire kumbuyo anthu oipa koma awaleke kuti awalange chifukwa cha zoipa zawo ndi kuti amene adamuchitirapo zoipa apeze bwino muntima mwake. Choncho aweruzi amilandu achenjere kukhalira kumbuyo anthu oipa omwe ali nawo chitsimikizo kuti adachenjelera anzawo. Asaone ulemelero wa munthu mmene ulili ngakhale ali ndi chuma chotani. Koma m’malomwake akhalire kumbuyo amene ali oponderezedwa. Akatero adzapeza mphoto yomwe Allah walonjeza chifukwa cha kusonyeza choonadi poyera. Aweruzi akagwira njira imeneyi ndiye kuti adzapambana pano padziko lapansi mpaka patsiku la chiweruziro.
Ərəbcə təfsirlər:
 
Mənaların tərcüməsi Ayə: (109) Surə: ən-Nisa
Surələrin mündəricatı Səhifənin rəqəmi
 
Qurani Kərimin mənaca tərcüməsi - Şişyo dilinə tərcümə - Tərcumənin mündəricatı

Qurani Kərimin şişyo dilinə mənaca tərcüməsi. Tərcüməçi:

Bağlamaq