ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا * - فهرس التراجم


ترجمة معاني آية: (118) سورة: النساء
لَّعَنَهُ ٱللَّهُۘ وَقَالَ لَأَتَّخِذَنَّ مِنۡ عِبَادِكَ نَصِيبٗا مَّفۡرُوضٗا
(Yemwe) Allah adamtembelera. Ndipo iye (satana) adati (kwa Allah): “Ndithudi, ndikadzipezera gawo lodziwika mwa akapolo anu.”[148]
[148] Iblis pamene adampirikitsa kumwamba iye adauza Allah kuti akazikometsera zolengedwa zake machimo. Allah adamuuza kuti sangathe kuzisokereza mwamphamvu, mozikakamiza, zifune zisafune. Aliyense amene akamtsata ndiye kuti akamtsata mwachifuniro chake. Sikuti mogonjetsedwa ndi mphamvu za satana kotero kuti iye sangathe kulimbana naye iyayi. Satana alibe mphamvu zokakamizira anthu.
التفاسير العربية:
 
ترجمة معاني آية: (118) سورة: النساء
فهرس السور رقم الصفحة
 
ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا - فهرس التراجم

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

إغلاق