Traducción de los significados del Sagrado Corán - Traducción al Chewa * - Índice de traducciones


Traducción de significados Versículo: (241) Capítulo: Sura Al-Baqara
وَلِلۡمُطَلَّقَٰتِ مَتَٰعُۢ بِٱلۡمَعۡرُوفِۖ حَقًّا عَلَى ٱلۡمُتَّقِينَ
Ndipo akazi osiidwa ukwati, apatsidwe chilekaniro chowasangalatsa m’chilamulo cha Shariya. Ili ndi lamulo kwa amene akuopa Allah.[42]
[42] Pamene mwamuna akumusiya mkazi ukwati pafunika kuti ampatse chinthu china kuwonjezera pa chiwongo. Koma Asilamu ambiri kudera la kuno kum’mawa kwa Afrika m’malo mompatsa chinthu mkazi pomusiya amaitanitsa chinthu kwamkazi kuti awapatse kapena kumlanda katundu kumene.
Machitidwe otere ngoipitsitsa, sali ogwirizana ndi malamulo a Chisilamu.
Las Exégesis Árabes:
 
Traducción de significados Versículo: (241) Capítulo: Sura Al-Baqara
Índice de Capítulos Número de página
 
Traducción de los significados del Sagrado Corán - Traducción al Chewa - Índice de traducciones

Traducción del significado del Corán al chewa por Khaled Ibrahim Betala (ed.2020)

Cerrar