Traducción de los significados del Sagrado Corán - Traducción al Chewa * - Índice de traducciones


Traducción de significados Versículo: (9) Capítulo: Sura Ash-Shams
قَدۡ أَفۡلَحَ مَن زَكَّىٰهَا
Ndithu wapambana amene wauyeretsa.[443]
[443] Kuyeretsa mzimu ndiko kuukongoletsa ndi maphunziro ndi ntchito zabwino. Zimenezi ndizo zimamkwanitsa munthu kuti atchulidwe munthu. Ndipo zimenezi ndizo zingapereke ulemelero kwa munthu pa dziko mpaka pa tsiku lachimaliziro.
Las Exégesis Árabes:
 
Traducción de significados Versículo: (9) Capítulo: Sura Ash-Shams
Índice de Capítulos Número de página
 
Traducción de los significados del Sagrado Corán - Traducción al Chewa - Índice de traducciones

Traducción del significado del Corán al chewa por Khaled Ibrahim Betala (ed.2020)

Cerrar