Fassarar Ma'anonin Alqura'ni - Fasaara da Yaren Pashto * - Teburin Bayani kan wasu Fassarori


Fassarar Ma'anoni Aya: (8) Sura: Suratu Al'nisaa
وَإِذَا حَضَرَ ٱلۡقِسۡمَةَ أُوْلُواْ ٱلۡقُرۡبَىٰ وَٱلۡيَتَٰمَىٰ وَٱلۡمَسَٰكِينُ فَٱرۡزُقُوهُم مِّنۡهُ وَقُولُواْ لَهُمۡ قَوۡلٗا مَّعۡرُوفٗا
Ndipo panthawi yogawa, ngati angabwere achibale, amasiye ndi osauka (omwe alibe gawo pa chumacho), apatseniko kanthu ndi kunena nawo mawu abwino.[111]
[111] Chuma nchinthu chimene chimachotsa moyo wa munthu mmalomwake, makamaka ngati chikupezeka m’njira yaulere yosachivutikira, monga chilili chuma chamasiye. Choncho amene alibepo gawo pa chumacho amangoti diso tong’o, kusilira. Ndipo nchifukwa chake Allah apa akunena kuti pogawa chuma chamasiyecho ngati achibale atabwerapo omwe alibepo gawo pa chumacho, awapatseko kachinthu kochepa ndi kuwapepesa kuti chomwe awapatsacho nchochepa.
Tafsiran larabci:
 
Fassarar Ma'anoni Aya: (8) Sura: Suratu Al'nisaa
Teburin Jerin Sunayen Surori Lambar shafi
 
Fassarar Ma'anonin Alqura'ni - Fasaara da Yaren Pashto - Teburin Bayani kan wasu Fassarori

Fassarar Maanonin Alurani mai girma zuwa Yaren shishiwa wanda Khalid Ibrahim Bitala kwafi na Shekarar 2020 Miladiyya

Rufewa