Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (172) Sura: Al ‘Imrân
ٱلَّذِينَ ٱسۡتَجَابُواْ لِلَّهِ وَٱلرَّسُولِ مِنۢ بَعۡدِ مَآ أَصَابَهُمُ ٱلۡقَرۡحُۚ لِلَّذِينَ أَحۡسَنُواْ مِنۡهُمۡ وَٱتَّقَوۡاْ أَجۡرٌ عَظِيمٌ
(Awa ndi) amene adavomera Allah ndi Mtumiki pambuyo povulazidwa; kwa amene achita zabwino mwa iwo ndi kuopa Allah, adzakhala ndi malipiro aakulu.[98]
[98] Asilamu makumi asanu ndi awiri (70) ataphedwa ndi enanso ochuluka atavulazidwa pa nkhondo ija ya Uhudi, Mtumiki (s.a.w) adawalamula Asilamu pompo, uku ali ndimabalawo, kuti awatsate adaniwo. Ndipo adawatsatadi. Koma adaniwo atamva mphekesera kuti akuwatsata naganiza kuti akutsatidwa ndi chigulu cha nkhondo cha Asilamu chachikulu, osati gulu lonlija lomwe adalipatsa mavuto. Choncho adaliyatsa liwiro kuthawa. Ndipo Asilamuwo adabwerera pambuyo poyenda mtunda wautali kuwatsata adaniwo. Tero Allah adawatamanda Asilamuwa pakumvera kwawo kumeneko.
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (172) Sura: Al ‘Imrân
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi