Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (37) Sura: An-Nisâ’
ٱلَّذِينَ يَبۡخَلُونَ وَيَأۡمُرُونَ ٱلنَّاسَ بِٱلۡبُخۡلِ وَيَكۡتُمُونَ مَآ ءَاتَىٰهُمُ ٱللَّهُ مِن فَضۡلِهِۦۗ وَأَعۡتَدۡنَا لِلۡكَٰفِرِينَ عَذَابٗا مُّهِينٗا
Omwe amachita umbombo ndi kulamula anthu kuchita umbombo ndi kubisa zabwino zomwe Allah wawapatsa. Komatu osakhulupirira tawakonzera chilango choyalutsa.[124]
[124] Kubisa zonse zomwe Allah wawapatsa kuli monga munthu kukhala ndi maphunziro koma osaphunzitsa anthu kotero kuti nkufa nawo popanda kuphunzitsapo aliyense. Kutero sibwino. Koma akafuna kukalowa m’Munda wa mtendere wa Allah nkofunika kuti achite zinthu zabwino ncholinga chokondweretsa Allah. Osati kuti anthu amuone ndi kumtama. Amene akuchita chinthu chabwino ncholinga choti anthu amtamande, sakalandira mphoto iliyonse pa tsiku lachimaliziro.
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (37) Sura: An-Nisâ’
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi