Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (11) Sura: Al-An‘âm
قُلۡ سِيرُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ ثُمَّ ٱنظُرُواْ كَيۡفَ كَانَ عَٰقِبَةُ ٱلۡمُكَذِّبِينَ
Nena: “Yendani pa dziko, kenako tayang’anani momwe adalili mapeto a otsutsa.” [170]
[170] Apa tanthauzo nkuti tayendani padziko mukayang’ane ndi kulingalira zilango zopweteka zimene zidawatsikira anthu akale. Kuyang’ana ndi kulingalira zoterezo kuti zikhale phunziro kwa inu kuti musachitenso zimene zidawagwetsa kuchionongeko.
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (11) Sura: Al-An‘âm
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi