Kilniojo Korano reikšmių vertimas - Čevų k. vertimas * - Vertimų turinys


Reikšmių vertimas Aja (Korano eilutė): (18) Sūra: Sūra Fatir
وَلَا تَزِرُ وَازِرَةٞ وِزۡرَ أُخۡرَىٰۚ وَإِن تَدۡعُ مُثۡقَلَةٌ إِلَىٰ حِمۡلِهَا لَا يُحۡمَلۡ مِنۡهُ شَيۡءٞ وَلَوۡ كَانَ ذَا قُرۡبَىٰٓۗ إِنَّمَا تُنذِرُ ٱلَّذِينَ يَخۡشَوۡنَ رَبَّهُم بِٱلۡغَيۡبِ وَأَقَامُواْ ٱلصَّلَوٰةَۚ وَمَن تَزَكَّىٰ فَإِنَّمَا يَتَزَكَّىٰ لِنَفۡسِهِۦۚ وَإِلَى ٱللَّهِ ٱلۡمَصِيرُ
Ndipo wosenza, sadzasenza mtolo wa wina. (Aliyense adzasenza mtolo wa machimo ake). Ngakhale amene walemedwa ndi mtolo wake ataitana (wina) chifukwa cha mtolo wake kuti amsenzere silidzatengedwa ngakhale gawo pang’ono la mtolowo (ndi munthu ameneyo), ngakhale atakhala m’bale wake. Ndithu ukuchenjeza okhawo amene akuopa Mbuye wawo pomwe sakumuona, ndipo akupemphera Swala moyenera, ndipo yemwe akudziyeretsa, ndithu akudziyeretsa yekha, (ubwino wake umubwerera iye mwini); ndipo mabwelero (a zolengedwa zonse) ndi kwa Allah (basi).
Tafsyrai arabų kalba:
 
Reikšmių vertimas Aja (Korano eilutė): (18) Sūra: Sūra Fatir
Sūrų turinys Puslapio numeris
 
Kilniojo Korano reikšmių vertimas - Čevų k. vertimas - Vertimų turinys

Kilniojo Korano reikšmių vertimas į čevų k., išvertė Khaled Ibrahim Betala. 2020 m. leidimas.

Uždaryti