Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling * - Index van vertaling


Vertaling van de betekenissen Vers: (127) Surah: Soerat Aal-Imraan ( Het Huis van Imraan )
لِيَقۡطَعَ طَرَفٗا مِّنَ ٱلَّذِينَ كَفَرُوٓاْ أَوۡ يَكۡبِتَهُمۡ فَيَنقَلِبُواْ خَآئِبِينَ
(Kuchita izi) nkuti adule gawo la osakhulupirira (kuti ena a iwo aphedwe) kapena awasambule ndi kuti abwelere ali olephera.[85]
[85] (Ndime 127-128) Apa Allah akufotokoza zifukwa zomwe adapambanitsira Asilamu. Ndipo akusonyeza ufumu Wake kuti chimene Iye wachifuna nchomwe chingachitike, osati chomwe auje ndi auje akufuna, ngakhale Mtumiki amene. Ngabodza omwe amati chimene akutiakuti afuna chimachitika, eti chifukwa choti iwowo ngolungama kwa Allah, kapena chifukwa chakuti ngoyera. Izi sizoona.
Arabische uitleg van de Qur'an:
 
Vertaling van de betekenissen Vers: (127) Surah: Soerat Aal-Imraan ( Het Huis van Imraan )
Surah's Index Pagina nummer
 
Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling - Index van vertaling

De vertaling van de betekenissen van de Heilige Quran in de Chewa-taal, vertaald door Khaled Ibrahim Bitalla. Editie van 2020.

Sluit