Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling * - Index van vertaling


Vertaling van de betekenissen Vers: (21) Surah: Soerat Saba (De Stad van Saba)
وَمَا كَانَ لَهُۥ عَلَيۡهِم مِّن سُلۡطَٰنٍ إِلَّا لِنَعۡلَمَ مَن يُؤۡمِنُ بِٱلۡأٓخِرَةِ مِمَّنۡ هُوَ مِنۡهَا فِي شَكّٖۗ وَرَبُّكَ عَلَىٰ كُلِّ شَيۡءٍ حَفِيظٞ
Ndipo iye adalibe nyonga pa iwo, koma chifukwa chakuti tionetse poyera ndani wokhulupirira tsiku la chimaliziro ndiponso ndani amene akulikaikira. Ndipo Mbuye wako Ngosunga chilichonse.[336]
[336] Pamene satana adatha kumsokeretsa Adam adaganizanso kuti adzatha kuwasokeretsa ana ake. Ndipo ana a Adam adamtsatiradi satanayo monga momwe iye ankaganizira. Komatu satana alibe mphamvu zomkakamizira mwana wa Adam kuti amtsate koma amangomuitana kupyolera m’kukometsera zilakolako zoipa.
Arabische uitleg van de Qur'an:
 
Vertaling van de betekenissen Vers: (21) Surah: Soerat Saba (De Stad van Saba)
Surah's Index Pagina nummer
 
Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling - Index van vertaling

De vertaling van de betekenissen van de Heilige Quran in de Chewa-taal, vertaald door Khaled Ibrahim Bitalla. Editie van 2020.

Sluit