Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling * - Index van vertaling


Vertaling van de betekenissen Vers: (110) Surah: Soerat An-nisa (de vrouwen)
وَمَن يَعۡمَلۡ سُوٓءًا أَوۡ يَظۡلِمۡ نَفۡسَهُۥ ثُمَّ يَسۡتَغۡفِرِ ٱللَّهَ يَجِدِ ٱللَّهَ غَفُورٗا رَّحِيمٗا
Ndipo amene angachite choipa (povutitsa ena), kapena kudzichitira yekha zoipa, kenako nkupempha chikhululuko kwa Allah, adzampeza Allah ali Wokhululuka kwabasi, Wachisoni chosatha. [144]
[144] Allah akuwalimbikitsa ochimwa: Kuti (a) atembenukire kwa Iye mwachangu ndi kusiya zimene akuchitazo. (b) Atsimikize mu mtima kuti sadzachitanso uchimowo. (c) Adandaule pa uchimo umene adauchitawo. (d) Awabwezere eni zinthu zomwe adazitenga mwachinyengo. (e) Akawapemphe kuti awakhululukire. Akakwaniritsa zonsezi ndiye kuti kulapa kwawo Allah akuvomera.
Arabische uitleg van de Qur'an:
 
Vertaling van de betekenissen Vers: (110) Surah: Soerat An-nisa (de vrouwen)
Surah's Index Pagina nummer
 
Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling - Index van vertaling

De vertaling van de betekenissen van de Heilige Quran in de Chewa-taal, vertaald door Khaled Ibrahim Bitalla. Editie van 2020.

Sluit