Tradução dos significados do Nobre Qur’an. - Tradução para a língua chachio * - Índice de tradução


Tradução dos significados Versículo: (112) Surah: Suratu An-Nisaa
وَمَن يَكۡسِبۡ خَطِيٓـَٔةً أَوۡ إِثۡمٗا ثُمَّ يَرۡمِ بِهِۦ بَرِيٓـٔٗا فَقَدِ ٱحۡتَمَلَ بُهۡتَٰنٗا وَإِثۡمٗا مُّبِينٗا
Ndipo amene angachite cholakwa (chaching’ono) kapena tchimo (lalikulu) kenako nkumponyera nalo yemwe sadalakwe (momunamizira), ndithudi wasenza bodza lamkunkhuniza ndi uchimo woonekera.[146]
[146] Pali anthu ena amene amaukwera uchimo. Kenako nkumnamizira wina wake. Munthu wamakhalidwe awa, chiweruzo chake chidzakhala choopsa tsiku lachimaliziro, ngakhale wadzipulumutsa pano pa dziko lapansi chifukwa chakuthyathyalika kwake. Kapena pompano pa dziko lapansi amachiona chomwe chinameta nkhanga mpala.
Os Tafssir em língua árabe:
 
Tradução dos significados Versículo: (112) Surah: Suratu An-Nisaa
Índice de capítulos Número de página
 
Tradução dos significados do Nobre Qur’an. - Tradução para a língua chachio - Índice de tradução

Tradução de significados do Nobre Al-Qur'án para a língua Chichio, traduzido por Khalid Ibrahim Bitálá. Edição do ano 2020

Fechar