Përkthimi i kuptimeve të Kuranit Fisnik - الترجمة الشيشيوا * - Përmbajtja e përkthimeve


Përkthimi i kuptimeve Ajeti: (108) Surja: Suretu En Nisa
يَسۡتَخۡفُونَ مِنَ ٱلنَّاسِ وَلَا يَسۡتَخۡفُونَ مِنَ ٱللَّهِ وَهُوَ مَعَهُمۡ إِذۡ يُبَيِّتُونَ مَا لَا يَرۡضَىٰ مِنَ ٱلۡقَوۡلِۚ وَكَانَ ٱللَّهُ بِمَا يَعۡمَلُونَ مُحِيطًا
Akudzibisa kwa anthu (pochita za machimo) koma sakuzibisa kwa Allah pomwe Iye adali nawo pamodzi pamene adali kupangana usiku mawu osakondweretsa. Allah akudziwa bwinobwino zimene akuchita.[142]
[142] Achiphamaso amabisa zochita zawo kwa anthu kuti asazione. Koma salabadira kuonedwa ndi Allah pomwe Allah Njemwe adzawalipira. Pomwe Allah akudziwa zonse zimene zikuyenda m’mitima mwawo ndiponso akumva ndi kuziona zonse zimene akuchita. Kunali kofunika kwa iwo kumuopa Allah amene ali ndi mphamvu zochitira chilichonse chimene wafuna.
Tefsiret në gjuhën arabe:
 
Përkthimi i kuptimeve Ajeti: (108) Surja: Suretu En Nisa
Përmbajtja e sureve Numri i faqes
 
Përkthimi i kuptimeve të Kuranit Fisnik - الترجمة الشيشيوا - Përmbajtja e përkthimeve

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

Mbyll