Kur'an-ı Kerim meal tercümesi - الترجمة الشيشيوا * - Mealler fihristi


Anlam tercümesi Ayet: (42) Sure: Sûratu'l-Ahzâb
وَسَبِّحُوهُ بُكۡرَةٗ وَأَصِيلًا
Ndipo mulemekezeni m’mawa ndi madzulo.[328]
[328] Allah wasankha nthawi ziwiri kuti zikhale zochulukitsa kumtamanda ndi kumulemekeza chifukwa chakuti zimenezi ndi nthawi zabwino zimene angelo amatsika kuchokera kumwamba.
Arapça tefsirler:
 
Anlam tercümesi Ayet: (42) Sure: Sûratu'l-Ahzâb
Surelerin fihristi Sayfa numarası
 
Kur'an-ı Kerim meal tercümesi - الترجمة الشيشيوا - Mealler fihristi

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

Kapat