クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (42) 章: 部族連合章
وَسَبِّحُوهُ بُكۡرَةٗ وَأَصِيلًا
Ndipo mulemekezeni m’mawa ndi madzulo.[328]
[328] Allah wasankha nthawi ziwiri kuti zikhale zochulukitsa kumtamanda ndi kumulemekeza chifukwa chakuti zimenezi ndi nthawi zabwino zimene angelo amatsika kuchokera kumwamba.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (42) 章: 部族連合章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる