Kodi sukuwaona omwe apatsidwa gawo la nzeru zozindikira buku (la Allah)? Amakhulupirira mafano ndi asatana, ndipo akumati kwa amene sadakhulupirire: “Awa ali panjira yoongoka kwabasi kuposa okhulupirira (Asilamu).”[127]
[127] Mawu oti “Jibti ndi Twaghut’’ amanena za chinthu chomwe anthu akuchipembedza chamoyo kapena chakufa chomwe sichili Mulungu weniweni monga momwe lilili dzina loti Shaytan. Iloli limatchulidwa kwa aliyense amene akusokeretsa anthu ku njira ya Allah. Chifukwa cha kuipidwa ndi Asilamu, Ayuda adapita ku Makka kukapalana ubwenzi ndi Aquraish ndi Arabu ena opembedza mafano kuti athandizane nawo kumthira nkhondo Mtumiki Muhammad (s.a.w) pamodzi ndi omtsatira ake kuti achithetseretu chipembedzo cha Chisilamu. Choncho akuluakulu a Chiyuda atafika ku Makka adagwadira mafano ncholinga chofuna kukondweretsa Aquraish pomwe Ayudawo adali eni mabuku omwe salola kupembedza mafano. Adawalimbikitsanso Aquraish aja powauza kuti: “Zochita zanu pa chipembedzo chanu nzabwino kuposa zochita za Muhammad pachipembedzo chake chimene wadza nacho.” Iwo amanena izi akudziwa kuti akunama. Cholinga chawo kudali kupeza chithandizo kwa iwo kuti athetse Chisilamu chifukwa chakudzadzidwa ndi njiru m’mitima mwawo ponena kuti: “Nchotani kuti Muhammad (s.a.w) alandire chisomo chauneneri?” Iwo ankachita izi ngati kuti ufumu wa Allah udali m’manja mwawo kuti iwo ndi amene amagawa zachifundo cha Allah, chonsecho, Allah amapereka kwa yemwe wamfuna. Iye amachita chimene wafuna. Safunsidwa ndi aliyense pa chimene wachita. Koma iwo amafunsidwa.
Contents of the translations can be downloaded and re-published, with the following terms and conditions:
1. No modification, addition, or deletion of the content.
2. Clearly referring to the publisher and the source (QuranEnc.com).
3. Mentioning the version number when re-publishing the translation.
4. Keeping the transcript information inside the document.
5. Notifying the source (QuranEnc.com) of any note on the translation.
6. Updating the translation according to the latest version issued from the source (QuranEnc.com).
7. Inappropriate advertisements must not be included when displaying translations of the meanings of the Noble Quran.
ئىزدەش نەتىجىسى:
API specs
Endpoints:
Sura translation
GET / https://quranenc.com/api/v1/translation/sura/{translation_key}/{sura_number} description: get the specified translation (by its translation_key) for the speicified sura (by its number)
Parameters: translation_key: (the key of the currently selected translation) sura_number: [1-114] (Sura number in the mosshaf which should be between 1 and 114)
Returns:
json object containing array of objects, each object contains the "sura", "aya", "translation" and "footnotes".
GET / https://quranenc.com/api/v1/translation/aya/{translation_key}/{sura_number}/{aya_number} description: get the specified translation (by its translation_key) for the speicified aya (by its number sura_number and aya_number)
Parameters: translation_key: (the key of the currently selected translation) sura_number: [1-114] (Sura number in the mosshaf which should be between 1 and 114) aya_number: [1-...] (Aya number in the sura)
Returns:
json object containing the "sura", "aya", "translation" and "footnotes".