قرآن کریم کے معانی کا ترجمہ - شیشیوا ترجمہ۔ * - ترجمے کی لسٹ


معانی کا ترجمہ آیت: (226) سورت: سورۂ بقرہ
لِّلَّذِينَ يُؤۡلُونَ مِن نِّسَآئِهِمۡ تَرَبُّصُ أَرۡبَعَةِ أَشۡهُرٖۖ فَإِن فَآءُو فَإِنَّ ٱللَّهَ غَفُورٞ رَّحِيمٞ
Kwa omwe akulumbilira kuti adzipatula kwa akazi awo, (nyengo yawo) ayembekezere miyezi inayi. Koma ngati atabwerera (nakhala pamodzi ndi akazi awo), ndithudi Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngwachisoni zedi. [34]
[34] Mwamuna akalumbira kuti sakhala naye pamodzi mkazi wake, tero mkaziyo ayembekezere nthawi yamiyezi inayi. Ndipo ngati nthawiyi ipambana asanakhalebe naye pamodzi, apite akamsumire kwa Kadhwi (mkulu wodziwa malamulo a Chisilamu). Ndipo Kadhwiyo akakamize mwamunayo kuti akhale naye pamodzi mkazi wakeyo, apo ayi, awalekanitse ngati izo zitalephereka. Sibwino kuvutitsana pakati pa anthu makamaka pakati pa mwamuna ndi mkazi.
عربی تفاسیر:
 
معانی کا ترجمہ آیت: (226) سورت: سورۂ بقرہ
سورتوں کی لسٹ صفحہ نمبر
 
قرآن کریم کے معانی کا ترجمہ - شیشیوا ترجمہ۔ - ترجمے کی لسٹ

قرآن کریم کے معانی کا شیشیوا ترجمہ، ترجمہ خالد ابراہیم بيتلا نے کیا ہے۔نسخہ ۲۰۲۰م۔

بند کریں