Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa * - Lexique des traductions


Traduction des sens Verset: (6) Sourate: AL-AN’ÂM
أَلَمۡ يَرَوۡاْ كَمۡ أَهۡلَكۡنَا مِن قَبۡلِهِم مِّن قَرۡنٖ مَّكَّنَّٰهُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ مَا لَمۡ نُمَكِّن لَّكُمۡ وَأَرۡسَلۡنَا ٱلسَّمَآءَ عَلَيۡهِم مِّدۡرَارٗا وَجَعَلۡنَا ٱلۡأَنۡهَٰرَ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهِمۡ فَأَهۡلَكۡنَٰهُم بِذُنُوبِهِمۡ وَأَنشَأۡنَا مِنۢ بَعۡدِهِمۡ قَرۡنًا ءَاخَرِينَ
Kodi saona kuti ndi mibadwo ingati tidaiononga patsogolo pawo? Tidawapatsa mphamvu yopezera za m’dziko zomwe sitidakupatseni inu. Ndipo tidawavumbwitsira mvula yopitiriza (mwa ubwino choncho, adasangalala kopambana). Ndipo tidaipanga mitsinje kuyenda pansi pawo (pansi pa mitengo yawo ndi nyumba zawo). Kenako tidawaononga chifukwa cha machimo awo, ndipo pambuyo pawo tidalenga mibadwo ina.
Les exégèses en arabe:
 
Traduction des sens Verset: (6) Sourate: AL-AN’ÂM
Lexique des sourates Numéro de la page
 
Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa - Lexique des traductions

Traduction des sens du noble Coran en langue chewa, par Khâlid Ibrâhîm Bîtâlâ (édition 2020).

Fermeture