Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa * - Lexique des traductions


Traduction des sens Verset: (8) Sourate: AL-A’LÂ
وَنُيَسِّرُكَ لِلۡيُسۡرَىٰ
Ndipo tikufewetsera (njira yochitira zinthu) zabwino.[420]
[420] Tanthauzo la ‘kufewetsa’ ndiko kuti Shariya ya Chisilamu (malamulo) siili yovuta kuyikwaniritsa monga momwe adalili malamulo a zipembedzo zoyamba. Ndipo ndi malamulo othandiza anthu onse, nthawi zonse ndi pamalo paliponse.
Les exégèses en arabe:
 
Traduction des sens Verset: (8) Sourate: AL-A’LÂ
Lexique des sourates Numéro de la page
 
Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa - Lexique des traductions

Traduction des sens du noble Coran en langue chewa, par Khâlid Ibrâhîm Bîtâlâ (édition 2020).

Fermeture