Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa * - Lexique des traductions


Traduction des sens Verset: (25) Sourate: AT-TAWBAH
لَقَدۡ نَصَرَكُمُ ٱللَّهُ فِي مَوَاطِنَ كَثِيرَةٖ وَيَوۡمَ حُنَيۡنٍ إِذۡ أَعۡجَبَتۡكُمۡ كَثۡرَتُكُمۡ فَلَمۡ تُغۡنِ عَنكُمۡ شَيۡـٔٗا وَضَاقَتۡ عَلَيۡكُمُ ٱلۡأَرۡضُ بِمَا رَحُبَتۡ ثُمَّ وَلَّيۡتُم مُّدۡبِرِينَ
Ndithu Allah wakhala akukupulumutsani (kwa adani anu) m’malo ambiri omenyanira nkhondo, ndi pa tsiku la Hunaini, pamene kudakunyengani kuchuluka kwanu. Koma sikudakuthandizeni chilichonse. Ndipo dziko lidakupanani ngakhale kuti lidali lotambasuka ndipo kenako mudatembenukira kumbuyo (kuthawa).[206]
[206] Apa Allah akuwakumbutsa Asilamu kuti wakhala akuwapulumutsa m’nkhondo zosiyanasiyana, makamaka pa nkhondo ya Hunaini pamene Asilamu adali kudzitama kuti sangagonjetsedwe chifukwa cha kuchuluka kwawo. Koma kuchulukako sikudawathandize chilichonse. Nthawi zonse chofunika kwa Msilamu nkudalira Allah. Asadalire mphamvu zake, chuma kapena zina zotero.
Les exégèses en arabe:
 
Traduction des sens Verset: (25) Sourate: AT-TAWBAH
Lexique des sourates Numéro de la page
 
Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa - Lexique des traductions

Traduction des sens du noble Coran en langue chewa, par Khâlid Ibrâhîm Bîtâlâ (édition 2020).

Fermeture