क़ुरआन के अर्थों का अनुवाद - चेवा अनुवाद * - अनुवादों की सूची


अर्थों का अनुवाद आयत: (5) सूरा: सूरा अल्-अन्फ़ाल
كَمَآ أَخۡرَجَكَ رَبُّكَ مِنۢ بَيۡتِكَ بِٱلۡحَقِّ وَإِنَّ فَرِيقٗا مِّنَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ لَكَٰرِهُونَ
Monga mmene Mbuye wako adakulamulira kutuluka m’nyumba yako (kupita ku Badr kukachita nkhondo ndi osakhulupirira) mwachoonadi, ndithu gulu lina la okhulipirira silidafune (kuchoka kukakumana ndi adani).[191]
[191] Pamene Asilamu adauzidwa kukakumana ndi Aquraish kuti akamenyane nawo nkhondo, ena mwa Asilamu adachita mantha chifukwa chakuti nthawiyi idali yoyamba kwa iwo kuuzidwa zokamenyana ndi adani awo, poganiziranso kuti Aquraish adali akatswiri pomenya nkhondo, ndiponso adali ochuluka zedi kuposa iwo. Choncho Asilamu adayesera kupereka madandaulo awa ndi awa.
अरबी तफ़सीरें:
 
अर्थों का अनुवाद आयत: (5) सूरा: सूरा अल्-अन्फ़ाल
सूरों की सूची पृष्ठ संख्या
 
क़ुरआन के अर्थों का अनुवाद - चेवा अनुवाद - अनुवादों की सूची

पवित्र क़ुरआन के अर्थों का चेवा अनुवाद। अनुवाद ख़ालिद अबराहीम बेताला ने किया है। प्रति वर्ष 2020 ईसवी।

बंद करें