Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (5) Sura: Al-Hashr
مَا قَطَعۡتُم مِّن لِّينَةٍ أَوۡ تَرَكۡتُمُوهَا قَآئِمَةً عَلَىٰٓ أُصُولِهَا فَبِإِذۡنِ ٱللَّهِ وَلِيُخۡزِيَ ٱلۡفَٰسِقِينَ
Sim’dadule mtengo uliwonse wa zipatso za kanjedza, (inu Asilamu), kapena kuusiya uli chiimire ndi thunthu lake koma nchifuniro cha Allah ndi kuti awayalutse otuluka m’malamulo Ake.[354]
[354] (Ndime 5-7) Ndime zimenezi zikufotokoza za kagawidwe ka chuma chosiyidwa ndi adani pankhondo. Chumacho sichongogawira amene amachita nkhondo okha ayi. Kapena kugawana akulu-akulu okha monga momwe amachitira ena omwe sali Asilamu pa nkhondo zawo. Chifukwa kutero ndiye kuti chumacho chizingozungulira pakati pa anthu olemera okhaokha. Chisilamu chikulamula kuti chuma choterechi chigawidwe kwa onse kuti umphawi uwachokere onse.
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (5) Sura: Al-Hashr
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi