Prijevod značenja časnog Kur'ana - الترجمة الشيشيوا * - Sadržaj prijevodā


Prijevod značenja Ajet: (5) Sura: Sura el-Hašr
مَا قَطَعۡتُم مِّن لِّينَةٍ أَوۡ تَرَكۡتُمُوهَا قَآئِمَةً عَلَىٰٓ أُصُولِهَا فَبِإِذۡنِ ٱللَّهِ وَلِيُخۡزِيَ ٱلۡفَٰسِقِينَ
Sim’dadule mtengo uliwonse wa zipatso za kanjedza, (inu Asilamu), kapena kuusiya uli chiimire ndi thunthu lake koma nchifuniro cha Allah ndi kuti awayalutse otuluka m’malamulo Ake.[354]
[354] (Ndime 5-7) Ndime zimenezi zikufotokoza za kagawidwe ka chuma chosiyidwa ndi adani pankhondo. Chumacho sichongogawira amene amachita nkhondo okha ayi. Kapena kugawana akulu-akulu okha monga momwe amachitira ena omwe sali Asilamu pa nkhondo zawo. Chifukwa kutero ndiye kuti chumacho chizingozungulira pakati pa anthu olemera okhaokha. Chisilamu chikulamula kuti chuma choterechi chigawidwe kwa onse kuti umphawi uwachokere onse.
Tefsiri na arapskom jeziku:
 
Prijevod značenja Ajet: (5) Sura: Sura el-Hašr
Indeks sura Broj stranice
 
Prijevod značenja časnog Kur'ana - الترجمة الشيشيوا - Sadržaj prijevodā

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

Zatvaranje