Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (9) Sura: Al-A‘lâ
فَذَكِّرۡ إِن نَّفَعَتِ ٱلذِّكۡرَىٰ
Choncho akumbutse (wanthu powalalikira) ngati kukumbutsa kuthandiza.[421]
[421] Tanthauzo la apa sikuti Mtumiki (s.a.w) alalikire pokhapokha waona kuti ulalikiwo uthandiza ayi, koma alalikire ndithu kaya kulalikirako kuthandiza kapena ayi, monga momwe zalongosolera Ayah zotsatirazi. Kuyankhula kotere, Arabu amakutcha “iktifa.”
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (9) Sura: Al-A‘lâ
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi