Check out the new design

《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 哈利德·伊布拉欣·比德拉。 * - 译解目录


含义的翻译 段: (9) 章: 艾尔拉
فَذَكِّرۡ إِن نَّفَعَتِ ٱلذِّكۡرَىٰ
Choncho akumbutse (wanthu powalalikira) ngati kukumbutsa kuthandiza.[421]
[421] Tanthauzo la apa sikuti Mtumiki (s.a.w) alalikire pokhapokha waona kuti ulalikiwo uthandiza ayi, koma alalikire ndithu kaya kulalikirako kuthandiza kapena ayi, monga momwe zalongosolera Ayah zotsatirazi. Kuyankhula kotere, Arabu amakutcha “iktifa.”
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (9) 章: 艾尔拉
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 哈利德·伊布拉欣·比德拉。 - 译解目录

由哈利德·伊布拉欣·白塔拉翻译。

关闭