Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa * - Indice Traduzioni


Traduzione dei significati Versetto: (5) Sura: Al-Qadr
سَلَٰمٌ هِيَ حَتَّىٰ مَطۡلَعِ ٱلۡفَجۡرِ
Mtendere usiku umenewo! (Palibe mavuto ndi zoipa) mpaka m’bandakucha.[465]
[465] Adanena Baidawi kuti tanthauzo la Ayah iyi ndikuti mu usiku umenewu Allah amalamula kuti kukhale mtendere wokhawokha. Koma mu usiku wina amalamula kuti kukhale mtendere ndi masoka.
Esegesi in lingua araba:
 
Traduzione dei significati Versetto: (5) Sura: Al-Qadr
Indice delle Sure Numero di pagina
 
Traduzione dei Significati del Sacro Corano - Traduzione chicheŵa - Indice Traduzioni

Traduzione dei significati del Nobile Corano in lingua chicheŵa, a cura di Khaled Ibrahim Beitala، ed. 2020

Chiudi