Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa * - Lexique des traductions


Traduction des sens Verset: (5) Sourate: AL-QADR
سَلَٰمٌ هِيَ حَتَّىٰ مَطۡلَعِ ٱلۡفَجۡرِ
Mtendere usiku umenewo! (Palibe mavuto ndi zoipa) mpaka m’bandakucha.[465]
[465] Adanena Baidawi kuti tanthauzo la Ayah iyi ndikuti mu usiku umenewu Allah amalamula kuti kukhale mtendere wokhawokha. Koma mu usiku wina amalamula kuti kukhale mtendere ndi masoka.
Les exégèses en arabe:
 
Traduction des sens Verset: (5) Sourate: AL-QADR
Lexique des sourates Numéro de la page
 
Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa - Lexique des traductions

Traduction des sens du noble Coran en langue chewa, par Khâlid Ibrâhîm Bîtâlâ (édition 2020).

Fermeture