クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (1) 章: 雌牛章

雌牛章

الٓمٓ
Alif-Lâm-Mîm.[1]
[1] Sura iyi yayamba ndi malembo a Alifabeti, monga Alif, Laam, Miim. kusonyeza kuti Qur’an yalembedwa ndi malembo amenewa omwe anthu amawagwiritsa ntchito m’zoyankhula ndi m’zolembalemba zawo. Uku ndikuwauza osakhulupilira kuti abweretse buku lawo lolembedwa ndi malembo omwe akuwadziwawo pamene iwo amanena kuti Qur’an adangoipeka yekha Muhammadi (s.a.w) siidavumbulutsidwe ndi Allah. Choncho Allah adawachalenja kuti alembe buku lawo lofanana ndi Qur’an, koma adalephera. Choncho, kulephera kwawo ndi umboni wosonyeza kuti Qur’an ndi buku lovumbulutsidwa ndi Allah.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (1) 章: 雌牛章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる