クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (5) 章: 物語章
وَنُرِيدُ أَن نَّمُنَّ عَلَى ٱلَّذِينَ ٱسۡتُضۡعِفُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ وَنَجۡعَلَهُمۡ أَئِمَّةٗ وَنَجۡعَلَهُمُ ٱلۡوَٰرِثِينَ
Ndipo tidafuna kuwachitira zabwino amene adafooketsedwa m’dziko (la Iguputo), ndi kuwachita kukhala atsogoleri ndi kuwachitanso kukhala amlowa mmalo ( a Baiti Al-Makadasi).[298]
[298] Chimene Allah wafuna chimachitika ngakhale anthu atayesetsa m’njira izi ndi izi kuti achizembe.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (5) 章: 物語章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる