クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (115) 章: イムラ―ン家章
وَمَا يَفۡعَلُواْ مِنۡ خَيۡرٖ فَلَن يُكۡفَرُوهُۗ وَٱللَّهُ عَلِيمُۢ بِٱلۡمُتَّقِينَ
Ndipo chabwino chilichonse chimene angachite sadzakanidwa nacho, (koma adzawalipira malipiro abwino). Ndipo Allah Ngodziwa za amene akuopa Iye.[79]
[79] Apa akunenetsa kuti aliyense amene akuchita zabwino ndicholinga chabwino ndi kutsata lamulo la Allah, adzalipidwa pa zabwino zakezo.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (115) 章: イムラ―ン家章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる