Check out the new design

クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim * - 対訳の目次


対訳 節: (55) 章: ビザンチン章
وَيَوۡمَ تَقُومُ ٱلسَّاعَةُ يُقۡسِمُ ٱلۡمُجۡرِمُونَ مَا لَبِثُواْ غَيۡرَ سَاعَةٖۚ كَذَٰلِكَ كَانُواْ يُؤۡفَكُونَ
Ndipo tsiku limene chiweruziro (Qiyâma) chidzachitika, oipa adzakhala akulumbira (kuti) sadakhale (pa dziko lapansi kapena mmanda) koma ola limodzi. Umo ndimomwe amatembenuzidwira (kuchokera ku njira ya choonadi).[309]
[309] Ndime iyi ikufotokozera kuti anthu ochita zoipa akadzaukitsidwa m’manda ndi kuona zoopsa zothetsa nzeru, adzaganiza kuti pamoyo wa padziko lapansi sadakhale nthawi yaitali koma ola limodzi basi. Izi nchifukwa chamavuto omwe adzakumana nawo patsiku limenelo.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (55) 章: ビザンチン章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim - 対訳の目次

カリード・イブラヒーム・ビタラの翻訳

閉じる