クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (11) 章: サバア章
أَنِ ٱعۡمَلۡ سَٰبِغَٰتٖ وَقَدِّرۡ فِي ٱلسَّرۡدِۖ وَٱعۡمَلُواْ صَٰلِحًاۖ إِنِّي بِمَا تَعۡمَلُونَ بَصِيرٞ
(Tidati kwa iye:) “Panga zovala (za chitsulo) zophanuka (zokwana thupi lonse, zodzitetezera pa nkhondo), ndipo linga bwino m’kulumikiza ndi poluka. Potero chitani zabwino. Ndithu Ine ndikuona zonse zimene mukuchita.”[333]
[333] Allah Wapamwambamwamba adamfewetsera Daud chitsulo kotero kuti adachisungunula nkusanduka ngati phala, napanga kuchokera m’phala limenelo zovala zodzitetezera pa nkhondo, ndiponso ziwiya zina zothandiza pa umoyo. Ichi chidali chisomo chachikulu chimene Allah adamdalitsa nacho iye pamodzi ndi ife tonse.
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (11) 章: サバア章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる