クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (5) 章: 創造者章
يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّاسُ إِنَّ وَعۡدَ ٱللَّهِ حَقّٞۖ فَلَا تَغُرَّنَّكُمُ ٱلۡحَيَوٰةُ ٱلدُّنۡيَا وَلَا يَغُرَّنَّكُم بِٱللَّهِ ٱلۡغَرُورُ
E inu anthu! Ndithu lonjezo la Allah ndi loona. Choncho usakunyengeni moyo wa dziko lapansi, ngakhale mdyerekezi uja wamkulu (Iblis), asakunyengeni pa za Allah.[339]
[339] M’ndime iyi Allah akutichenjeza kuti tisanyengedwe ndi malangizo a Satana akuti: “Chitani mmene mungafunire, Allah Wachifundo chambiri adzakukhululukirani.”
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (5) 章: 創造者章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる