クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (13) 章: 集合章
لَأَنتُمۡ أَشَدُّ رَهۡبَةٗ فِي صُدُورِهِم مِّنَ ٱللَّهِۚ ذَٰلِكَ بِأَنَّهُمۡ قَوۡمٞ لَّا يَفۡقَهُونَ
Ndithu inu (Asilamu) mukuopedwa kwambiri m’mitima mwawo kuposa mmene akumuopera Allah. Zimenezo nchifukwa chakuti iwo ndi anthu osazindikira (chilichonse).
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (13) 章: 集合章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる