クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (94) 章: 家畜章
وَلَقَدۡ جِئۡتُمُونَا فُرَٰدَىٰ كَمَا خَلَقۡنَٰكُمۡ أَوَّلَ مَرَّةٖ وَتَرَكۡتُم مَّا خَوَّلۡنَٰكُمۡ وَرَآءَ ظُهُورِكُمۡۖ وَمَا نَرَىٰ مَعَكُمۡ شُفَعَآءَكُمُ ٱلَّذِينَ زَعَمۡتُمۡ أَنَّهُمۡ فِيكُمۡ شُرَكَٰٓؤُاْۚ لَقَد تَّقَطَّعَ بَيۡنَكُمۡ وَضَلَّ عَنكُم مَّا كُنتُمۡ تَزۡعُمُونَ
Ndipo (tsiku la Qiyâma tidzakuuzani): “Ndithudi, mwatidzera mmodzimmodzi (payekhapayekha popanda chuma ndi ana kuti zikupulumutseni), monga mmene tidakulengerani pachiyambi. Ndipo mwasiya kumbuyo kwanu zonse zomwe tidakupatsani. Ndipo sitikuona pamodzi nanu apulumutsi anu aja, amene munkati ngothandizana (ndi Allah; ndi kuti iwo ndi apulumutsi anu). Ndithudi mgwirizano omwe udali pakati panu waduka. Ndipo zakusokonekerani zimene munkaziganizira (kuti ndi milungu).”
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (94) 章: 家畜章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる