クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (32) 章: 戦利品章
وَإِذۡ قَالُواْ ٱللَّهُمَّ إِن كَانَ هَٰذَا هُوَ ٱلۡحَقَّ مِنۡ عِندِكَ فَأَمۡطِرۡ عَلَيۡنَا حِجَارَةٗ مِّنَ ٱلسَّمَآءِ أَوِ ٱئۡتِنَا بِعَذَابٍ أَلِيمٖ
Ndipo (kumbukira) pamene adati: “E Inu Allah! Ngati ichi (chimene wadza nacho Muhammad {s.a.w}) chili choonadi chochokera kwa Inu, tivumbwitsireni mvula ya miyala yochokera kumwamba, kapena mutibweretsere chilango chowawa kwambiri.”[200]
[200] Ayah iyi ikusonyeza kuti sadali kuchifuna choonadi, chilungamo ndi zabwino zomwe adadza nazo Mneneri Muhammad (s.a.w).
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (32) 章: 戦利品章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる