クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (7) 章: 無花果章
فَمَا يُكَذِّبُكَ بَعۡدُ بِٱلدِّينِ
Tsono nchiyani chakuchititsa kuti ukanire kuuka ndi malipiro pambuyo (poona mphamvu zathu pa chilichonse)?[459]
[459] (Ndime 7-8) Allah akuuza munthu kuti: Pambuyo podziwa kuti Allah ndi Yemwe adapanga zimenezo, ndi chiyani nanga chikumukaikitsa za tsiku la chiweruziro?
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (7) 章: 無花果章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる