पवित्र कुरअानको अर्थको अनुवाद - चेवा अनुवाद * - अनुवादहरूको सूची


अर्थको अनुवाद श्लोक: (18) सूरः: सूरतुल् अअ्ला
إِنَّ هَٰذَا لَفِي ٱلصُّحُفِ ٱلۡأُولَىٰ
Ndithu izi (mukuuzidwa m’Qur’an) zilipo m’mabuku oyamba, akale,[424]
[424] Mawu akuti “wapambana amene wadziyeretsa ndi kumkumbukira Mbuye wake ndi kumapemphera,” ndiponso kuti: “ tsiku lachimaliziro ndilabwino kuposa dziko lapansi” mawuwa adanenedwanso m’mabuku oyamba; sikuti Qur’an ndiyo yayamba kunena zimenezi.
अरबी व्याख्याहरू:
 
अर्थको अनुवाद श्लोक: (18) सूरः: सूरतुल् अअ्ला
अध्यायहरूको (सूरःहरूको) सूची رقم الصفحة
 
पवित्र कुरअानको अर्थको अनुवाद - चेवा अनुवाद - अनुवादहरूको सूची

पवित्र कुर्आनको अर्थको चेवा भाषामा अनुवाद, अनुवादक : खालिद इब्राहीम बेताला, प्रकाशन : २०२० ।

बन्द गर्नुस्