Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling * - Index van vertaling


Vertaling van de betekenissen Vers: (14) Surah: Soerat Loqmaan (De Wijzen)
وَوَصَّيۡنَا ٱلۡإِنسَٰنَ بِوَٰلِدَيۡهِ حَمَلَتۡهُ أُمُّهُۥ وَهۡنًا عَلَىٰ وَهۡنٖ وَفِصَٰلُهُۥ فِي عَامَيۡنِ أَنِ ٱشۡكُرۡ لِي وَلِوَٰلِدَيۡكَ إِلَيَّ ٱلۡمَصِيرُ
Ndipo tamulangiza munthu kwa makolo ake (kuwachitira zabwino), mayi wake adatenga pathupi pake mofooka pamwamba pakufooka. (Adamuyamwitsa) ndi kumusiyitsa patapita zaka ziwiri, kuti: “Ndithokoze Ine ndi makolo ako, kwa Ine nkobwerera.” [312]
[312] M’ndime izi 14 mpaka 15 Allah akulamula munthu kuti achitire zabwino makolo ake powamvera ndi kuwathandiza ngati ali osowa. Izi nchifukwa cha kuti makolo ake adazunzika kwambiri pomulera iye makamaka mayi wake ndi amene adazunzika kwambiri kuyambira pamene adatenga mimba yake kufikira pamene adamusiyitsa kuyamwa. Choncho mverani makolo anu pazimene akukulangizani zomwe sizili zolakwira Allah. Koma ngati akukulangizani zolakwira Allah, musatsatire malangizo awowo, koma khalani nawoni mwa ubwino.
Arabische uitleg van de Qur'an:
 
Vertaling van de betekenissen Vers: (14) Surah: Soerat Loqmaan (De Wijzen)
Surah's Index Pagina nummer
 
Vertaling van de betekenissen Edele Qur'an - Chewa vertaling - Index van vertaling

De vertaling van de betekenissen van de Heilige Quran in de Chewa-taal, vertaald door Khaled Ibrahim Bitalla. Editie van 2020.

Sluit