د قرآن کریم د معناګانو ژباړه - چیچوایي ژباړه * - د ژباړو فهرست (لړلیک)


د معناګانو ژباړه آیت: (14) سورت: لقمان
وَوَصَّيۡنَا ٱلۡإِنسَٰنَ بِوَٰلِدَيۡهِ حَمَلَتۡهُ أُمُّهُۥ وَهۡنًا عَلَىٰ وَهۡنٖ وَفِصَٰلُهُۥ فِي عَامَيۡنِ أَنِ ٱشۡكُرۡ لِي وَلِوَٰلِدَيۡكَ إِلَيَّ ٱلۡمَصِيرُ
Ndipo tamulangiza munthu kwa makolo ake (kuwachitira zabwino), mayi wake adatenga pathupi pake mofooka pamwamba pakufooka. (Adamuyamwitsa) ndi kumusiyitsa patapita zaka ziwiri, kuti: “Ndithokoze Ine ndi makolo ako, kwa Ine nkobwerera.” [312]
[312] M’ndime izi 14 mpaka 15 Allah akulamula munthu kuti achitire zabwino makolo ake powamvera ndi kuwathandiza ngati ali osowa. Izi nchifukwa cha kuti makolo ake adazunzika kwambiri pomulera iye makamaka mayi wake ndi amene adazunzika kwambiri kuyambira pamene adatenga mimba yake kufikira pamene adamusiyitsa kuyamwa. Choncho mverani makolo anu pazimene akukulangizani zomwe sizili zolakwira Allah. Koma ngati akukulangizani zolakwira Allah, musatsatire malangizo awowo, koma khalani nawoni mwa ubwino.
عربي تفسیرونه:
 
د معناګانو ژباړه آیت: (14) سورت: لقمان
د سورتونو فهرست (لړلیک) د مخ نمبر
 
د قرآن کریم د معناګانو ژباړه - چیچوایي ژباړه - د ژباړو فهرست (لړلیک)

چیچوایي ژبې ته د قرآن کریم د معناګانو ژباړه، خالد ابراهیم بیتالا ژباړلې ده، ۲۰۲۰ کال چاپ

بندول