Salin ng mga Kahulugan ng Marangal na Qur'an - الترجمة الشيشيوا * - Indise ng mga Salin


Salin ng mga Kahulugan Ayah: (83) Surah: Tā-ha
۞ وَمَآ أَعۡجَلَكَ عَن قَوۡمِكَ يَٰمُوسَىٰ
“Nchiyani chakufulumizitsa (kudza kuno) kusiya anthu ako, E, iwe Mûsa?”[283]
[283] Imam Zamakhshari adati: “Musa pamodzi ndi nthumwi zomwe adazisankha zochokera mwa anthu ake, adamka ku phiri monga panyengo yomwe idaikidwa. Kenako iye adatsogola nasiya m’buyo anthu chifukwa chakhumbo ndi kufunitsitsa kumva mawu a Mbuye wake.”
Ang mga Tafsir na Arabe:
 
Salin ng mga Kahulugan Ayah: (83) Surah: Tā-ha
Indise ng mga Surah Numero ng Pahina
 
Salin ng mga Kahulugan ng Marangal na Qur'an - الترجمة الشيشيوا - Indise ng mga Salin

ترجمة معاني القرآن الكريم إلى اللغة الشيشيوا، ترجمها خالد إبراهيم بيتالا. نسخة عام 2020م.

Isara