《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 * - 译解目录


含义的翻译 段: (179) 章: 拜格勒
وَلَكُمۡ فِي ٱلۡقِصَاصِ حَيَوٰةٞ يَٰٓأُوْلِي ٱلۡأَلۡبَٰبِ لَعَلَّكُمۡ تَتَّقُونَ
Mu Qiswas (kubwezerana kofanana) muli kusunga moyo kwa inu, E, inu eni nzeru! Kuti mudzitchinjirize (ku mchitidwe ophana).[16]
[16] Muli moyo wabwino m’machitidwe abwino chifukwa chakuti potsata zimenezi aliyense adzakhala wotsata mwambo. Adzaopa kuti ngati apha mnzake nayenso aphedwa. Ngati achitira mnzake choipa nayenso amchitira choipa. Tero popewa zopwetekazo akhala ngati akusunga miyoyo ya anthu ena ndi wake womwe.
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (179) 章: 拜格勒
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 译解目录

古兰经契瓦文译解,哈利德·伊布拉欣·比德拉翻译,2020年版

关闭