《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 * - 译解目录


含义的翻译 段: (148) 章: 尼萨仪
۞ لَّا يُحِبُّ ٱللَّهُ ٱلۡجَهۡرَ بِٱلسُّوٓءِ مِنَ ٱلۡقَوۡلِ إِلَّا مَن ظُلِمَۚ وَكَانَ ٱللَّهُ سَمِيعًا عَلِيمًا
۞ Allah sakonda kutulutsa mawu ofalitsa kuipa (kwa anthu) kupatula yekhayo wachitiridwa zoipa. Ndipo Allah Ngwakumva, Ngodziwa.[151]
[151] Indedi, Allah sakonda anthu ofalitsa zoipa za anzawo popanda choipa chilichonse chimene awachitira. Koma munthu amene ena amchitira choipa akumlola kutchula kuipa komwe ena amchitira pokamnenera kwa muweruzi kuti muweruziyo amuthandize pa amene amchitira zoipawo. Koma kulengeza kuipa kwa anthu ena nkosaloledwa m’chisilamu. Ndipo ndi uchimo waukulu.
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (148) 章: 尼萨仪
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 译解目录

古兰经契瓦文译解,哈利德·伊布拉欣·比德拉翻译,2020年版

关闭