《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 * - 译解目录


含义的翻译 段: (150) 章: 尼萨仪
إِنَّ ٱلَّذِينَ يَكۡفُرُونَ بِٱللَّهِ وَرُسُلِهِۦ وَيُرِيدُونَ أَن يُفَرِّقُواْ بَيۡنَ ٱللَّهِ وَرُسُلِهِۦ وَيَقُولُونَ نُؤۡمِنُ بِبَعۡضٖ وَنَكۡفُرُ بِبَعۡضٖ وَيُرِيدُونَ أَن يَتَّخِذُواْ بَيۡنَ ذَٰلِكَ سَبِيلًا
Ndithudi amene sakhulupirira Allah ndi atumiki Ake, ndikumafuna kulekanitsa pakati pa Allah ndi atumiki Ake, ndikumanena kuti: “Ena tikuwakhulupirira, koma ena tikuwakana,” ndikumafunanso kukhonza njira yapakati pa zimenezo,[152]
[152] Aliyense mwa anthu yemwe Allah wamuvomereza kuti ndi mtumiki Wake, ndipo iwe nkukana kumkhulupilira, monga Ayuda mmene amamkanira mneneri Isa (Yesu), ndi Akhrisitu mmene amamkanira mneneri Muhammad (s.a.w), kutereko nkusakhulupilira Allah. Asilamu amavomereza aneneri onse owona amene adadza Muhammad (s.a.w) asadabadwe. Asilamu akuvomereza aneneri onse monga momwe Allah wafotokozera m’Qur’an. Ndipo savomereza omwe Allah sadawavomereze kuti ndi aneneri ake, monga Mirza Gulam Ahmad ndi Bahai. Oterewa ndi amene akunama kuti adapatsidwa uneneri pambuyo pa Mneneri Muhammad (s.a.w). Amene akukhulupilira amenewa ndiye kuti ngopandukira Allah. Tero tichenjere ndi udyerekezi wa Akadiani ndi Abahai ndi ena otere.
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (150) 章: 尼萨仪
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 译解目录

古兰经契瓦文译解,哈利德·伊布拉欣·比德拉翻译,2020年版

关闭