《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 * - 译解目录


含义的翻译 段: (7) 章: 艾奈尔姆
وَلَوۡ نَزَّلۡنَا عَلَيۡكَ كِتَٰبٗا فِي قِرۡطَاسٖ فَلَمَسُوهُ بِأَيۡدِيهِمۡ لَقَالَ ٱلَّذِينَ كَفَرُوٓاْ إِنۡ هَٰذَآ إِلَّا سِحۡرٞ مُّبِينٞ
Ndipo ngati tikadakutsitsira malemba (olembedwa) m’mapepala, (monga momwe adakufunsira), nkuwakhudza ndi manja awo, amene sadakhulupirire akadati: “Ichi sichina koma ndi matsenga owoneka.”
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (7) 章: 艾奈尔姆
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 译解目录

古兰经契瓦文译解,哈利德·伊布拉欣·比德拉翻译,2020年版

关闭