《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 * - 译解目录


含义的翻译 段: (3) 章: 艾尔拉
وَٱلَّذِي قَدَّرَ فَهَدَىٰ
Amene adalamuliratu (chilichonse zochita zake) ndi kuchiongolera.[418]
[418] Allah pambuyo polenga zolengedwa Zake sadangozileka kuti zisadziwe chochita, koma cholengedwa chilichonse adachilamuliratu kuti chichite zoyenera nacho, ndipo pambuyo pake adachiongolera pa chinthu chimenecho; chidadziwa, ndipo chidachita. Munthu adamusonyeza zomwe zili ndi mazunzo mkati mwake kuti adzitalikitse nazo ndiponso adamusonyeza zabwino kuti azichite.
阿拉伯语经注:
 
含义的翻译 段: (3) 章: 艾尔拉
章节目录 页码
 
《古兰经》译解 - 契瓦语翻译 - 译解目录

古兰经契瓦文译解,哈利德·伊布拉欣·比德拉翻译,2020年版

关闭