للإطلاع على الموقع بحلته الجديدة

ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا - خالد إبراهيم بتيالا * - فهرس التراجم


ترجمة معاني آية: (72) سورة: آل عمران
وَقَالَت طَّآئِفَةٞ مِّنۡ أَهۡلِ ٱلۡكِتَٰبِ ءَامِنُواْ بِٱلَّذِيٓ أُنزِلَ عَلَى ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَجۡهَ ٱلنَّهَارِ وَٱكۡفُرُوٓاْ ءَاخِرَهُۥ لَعَلَّهُمۡ يَرۡجِعُونَ
Ndipo gulu lina la amene adapatsidwa buku lidati (kwa anzawo): “Khulupirirani chomwe chavumbulutsidwa kwa Asilamu kumayambiliro kwa usana, ndipo chikaneni kumalekezero kwake (kwa usana) mwina angabwelere (kusiya Chisilamu).[73]
[73] Ena mwa anthu a mabuku adalangizana pakati pawo kuti chikhulupirire chipembedzo cha Chisilamu nthawi zakummawa zokha. Ikakwana nthawi yopemphera Swala akapemphere nawo. Koma ikafika nthawi yamadzulo atuluke m’chipembedzocho ncholinga choti asokoneze Asilamu maganizo, makamaka omwe adali ofooka pomwe aone kuti anthu anzeru adalowa m’chipembedzocho, koma kenako atulukamo, nawonso mwina atuluka poganiza kuti chikadakhala chipembedzo chenicheni anthu anzeru sakadatulukamo. Izi zidali ndale za Ayuda zomwe Allah adaziulula.
التفاسير العربية:
 
ترجمة معاني آية: (72) سورة: آل عمران
فهرس السور رقم الصفحة
 
ترجمة معاني القرآن الكريم - الترجمة الشيشيوا - خالد إبراهيم بتيالا - فهرس التراجم

ترجمها خالد إبراهيم بيتالا.

إغلاق